Osewera wakale wa timu ya Dedza Young Soccer Chisomo Mpachika wa m’boma la Dedza ndi m’modzi mwa osewera omwe awoneka kuzokonzekera zoyamba za timu ya Masters Security FC.
Mpachika yemwe wakhala nthawi yayitali ali ndi timu ya Silver Strikers, ndi m’modzi mwa osewera odziwika bwino omwe mphunzitsi wakale wa matimu a Silver Strikers komanso FCB Nyasa Big Bullets Peter Mponda yemwe akutsogolera timu ya Masters padakali pano anawafuna kuti akhale nawo ku timuyi.
Timu ya Masters Security FC ikubweleranso mu ligi yayikulu m’dziko muno itagula malo osewera mu ligiyi kuchoka ku timu ya Baka City ya m’chigawo chakumpoto.
WAYAMBA NAWO ZOKOZEKERA -MPACHIKA
86
previous post